Sitikukana kuvomereza bajeti-Katsonga
PHUNGU wa nyumba ya malamulo woimira dera la kum’mwera m’boma la Neno, a Mark Katsonga Phiri, loweruka sabata latha adauza anthu a m’dera lake kuti aphungu wochokera mu zipani zotsutsa boma m’dziko muno sakukana kuvomereza ndondomeko ya momwe boma...
Read More

Bullets ikumananso ndi Manoma mawa
MAWA kulinso masewero a nkhodzo za pusi pamene matimu a MTL Wanderers ndi Big Bullets akukumananso pa bwalo la za masewero la Kamuzu mu mzinda wa Blantyre. Masewerowo...
 
TIKAMBE ZA EDZI: Sabata lokumbukira za Edzi lithandiza kwenikweni
NDIRI ndi chikhulupiliro kuti chaka chatha nkhani imeneyi ndidakambaponso powunikira ubwino woyezetsa magazi ndi kudziwa zotsatira ngati munthu ali...
 
Timu ya VTC Thunders iteteza chikho cha Old Mutual
TIMU ya VTC Thunders idateteza chikho cha masewero a volebo omwe imathandiza ndi kampani ya Old Mutual itangonjetsa timu ya VTC Veterans ndi zigoli...
 
Apempha mabungwe athandize asilikali odwala Edzi
MKULU woyanga’anira za matenda a Edzi m’malo a asilikali a Cobbe Baracks m’boma la Zomba a Joseph Mdzinga adapempha mabungwe onse akufuna kwabwino...
 
‘Tidzipereka kulimbikitsa maphunziro a ana amasiye’
BUNGWE lothandiza ana amasiye la Carlos Cepeda Foundation lati lizipereka poyesetsa kutukula maphunziro a ana amasiye m’dziko muno pothandiza kupereka...
 



 

Group Publications :


Website Redesigned and Hosted by